Quantcast
Viewing all articles
Browse latest Browse all 3254

‘Kulira kwake ndiye nkumatani abale?’ Chipani cha UTM chalira kumwalira kwa Lucius Banda

Chipani cha UTM chati imfa ya Soldier Lucius Banda mnjowawa kwambiri maka pomwe chipanichi chikulirabe mtsogoleri wawo a Saulos Chilima. Lucius Banda anali mkulu okopa (Campaign Director) anthu mchipani cha UTM. Mneneri wa UTM a Felix Njawala wati ngati chipani sakudziwa kuti nkumatanino ndi momwe imfa yatengera akuluakulu ake motsogozana. Afotokoza a Njawala: “Pomwe a […]

The post ‘Kulira kwake ndiye nkumatani abale?’ Chipani cha UTM chalira kumwalira kwa Lucius Banda appeared first on Malawi Nyasa Times - News from Malawi about Malawi.

Viewing all articles
Browse latest Browse all 3254

Trending Articles



<script src="https://jsc.adskeeper.com/r/s/rssing.com.1596347.js" async> </script>